Add parallel Print Page Options

Anthu Oyimba Nyimbo

25 Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:

Kuchokera kwa ana a Asafu:

Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.

Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake:

Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.

Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake:

Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti. Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.

Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu. Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288. Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.

Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe,
ana ndi abale ake.12
Maere achiwiri anagwera Gedaliya,
ndi abale ake ndi ana ake.12
10 Maere achitatu anagwera Zakuri,
ana ake ndi abale ake.12
11 Maere achinayi anagwera Iziri,
ana ake ndi abale ake.12
12 Maere achisanu anagwera Netaniya,
ana ake ndi abale ake.12
13 Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya,
ana ake ndi abale ake.12
14 Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela,
ana ake ndi abale ake.12
15 Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya,
ana ake ndi abale ake.12
16 Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya,
ana ake ndi abale ake.12
17 Maere a khumi anagwera Simei,
ana ake ndi abale ake.12
18 Maere a 11 anagwera Azareli,
ana ake ndi abale ake.12
19 Maere a 12 anagwera Hasabiya,
ana ake ndi abale ake.12
20 Maere a 13 anagwera Subaeli,
ana ake ndi abale ake.12
21 Maere a 14 anagwera Matitiya,
ana ake ndi abale ake.12
22 Maere a 15 anagwera Yeremoti,
ana ake ndi abale ake.12
23 Maere a 16 anagwera Hananiya,
ana ake ndi abale ake.12
24 Maere a 17 anagwera Yosibakasa,
ana ake ndi abale ake.12
25 Maere a 18 anagwera Hanani,
ana ake ndi abale ake.12
26 Maere a 19 anagwera Maloti,
ana ake ndi abale ake.12
27 Maere a 20 anagwera Eliyata,
ana ake ndi abale ake.12
28 Maere a 21 anagwera Hotiri,
ana ake ndi abale ake.12
29 Maere a 22 anagwera Gidaliti,
ana ake ndi abale ake.12
30 Maere a 23 anagwera Mahazioti,
ana ake ndi abale ake.12
31 Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri,
ana ake ndi abale ake12.

The Musicians

25 David, together with the commanders of the army, set apart some of the sons of Asaph,(A) Heman(B) and Jeduthun(C) for the ministry of prophesying,(D) accompanied by harps, lyres and cymbals.(E) Here is the list of the men(F) who performed this service:(G)

From the sons of Asaph:

Zakkur, Joseph, Nethaniah and Asarelah. The sons of Asaph were under the supervision of Asaph, who prophesied under the king’s supervision.

As for Jeduthun, from his sons:(H)

Gedaliah, Zeri, Jeshaiah, Shimei,[a] Hashabiah and Mattithiah, six in all, under the supervision of their father Jeduthun, who prophesied, using the harp(I) in thanking and praising the Lord.

As for Heman, from his sons:

Bukkiah, Mattaniah, Uzziel, Shubael and Jerimoth; Hananiah, Hanani, Eliathah, Giddalti and Romamti-Ezer; Joshbekashah, Mallothi, Hothir and Mahazioth. (All these were sons of Heman the king’s seer. They were given him through the promises of God to exalt him. God gave Heman fourteen sons and three daughters.)

All these men were under the supervision of their father(J) for the music of the temple of the Lord, with cymbals, lyres and harps, for the ministry at the house of God.

Asaph, Jeduthun and Heman(K) were under the supervision of the king.(L) Along with their relatives—all of them trained and skilled in music for the Lord—they numbered 288. Young and old alike, teacher as well as student, cast lots(M) for their duties.

The first lot, which was for Asaph,(N) fell to Joseph,
his sons and relatives[b]12[c]
the second to Gedaliah,
him and his relatives and sons12
10 the third to Zakkur,
his sons and relatives12
11 the fourth to Izri,[d]
his sons and relatives12
12 the fifth to Nethaniah,
his sons and relatives12
13 the sixth to Bukkiah,
his sons and relatives12
14 the seventh to Jesarelah,[e]
his sons and relatives12
15 the eighth to Jeshaiah,
his sons and relatives12
16 the ninth to Mattaniah,
his sons and relatives12
17 the tenth to Shimei,
his sons and relatives12
18 the eleventh to Azarel,[f]
his sons and relatives12
19 the twelfth to Hashabiah,
his sons and relatives12
20 the thirteenth to Shubael,
his sons and relatives12
21 the fourteenth to Mattithiah,
his sons and relatives12
22 the fifteenth to Jerimoth,
his sons and relatives12
23 the sixteenth to Hananiah,
his sons and relatives12
24 the seventeenth to Joshbekashah,
his sons and relatives12
25 the eighteenth to Hanani,
his sons and relatives12
26 the nineteenth to Mallothi,
his sons and relatives12
27 the twentieth to Eliathah,
his sons and relatives12
28 the twenty-first to Hothir,
his sons and relatives12
29 the twenty-second to Giddalti,
his sons and relatives12
30 the twenty-third to Mahazioth,
his sons and relatives12
31 the twenty-fourth to Romamti-Ezer,
his sons and relatives12.(O)

Footnotes

  1. 1 Chronicles 25:3 One Hebrew manuscript and some Septuagint manuscripts (see also verse 17); most Hebrew manuscripts do not have Shimei.
  2. 1 Chronicles 25:9 See Septuagint; Hebrew does not have his sons and relatives.
  3. 1 Chronicles 25:9 See the total in verse 7; Hebrew does not have twelve.
  4. 1 Chronicles 25:11 A variant of Zeri
  5. 1 Chronicles 25:14 A variant of Asarelah
  6. 1 Chronicles 25:18 A variant of Uzziel